Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 4:16 - Buku Lopatulika

16 Lamulira ansembe akusenza likasa la umboni, kuti akwere kutuluka mu Yordani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Lamulira ansembe akusenza likasa la umboni, kuti akwere kutuluka m'Yordani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 “Lamula ansembe onyamula Bokosi lachipanganowo, kuti atuluke m'madzimo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 “Lamula ansembe onyamula Bokosi la Chipanganowo kuti atuluke mu Yorodani.”

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 4:16
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Yoswa,


Pamenepo Yoswa analamulira ansembe, ndi kuti, Kwerani kutuluka mu Yordani.


Ndipo anatsegulidwa Kachisi wa Mulungu amene ali mu Mwamba; ndipo linaoneka likasa la chipangano chake, mu Kachisi mwake, ndipo panali mphezi, ndi mau, ndi mabingu, ndi chivomezi, ndi matalala aakulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa