Yoswa 4:13 - Buku Lopatulika13 ngati zikwi makumi anai ankhondo okonzeka anaoloka pamaso pa Yehova kuthira nkhondo ku zidikha za Yeriko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ngati zikwi makumi anai ankhondo okonzeka anaoloka pamaso pa Yehova kuthira nkhondo ku zidikha za Yeriko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Asilikali ngati zikwi makumi anai adaoloka, nakaima pa tsidya, m'chigwa cha Yeriko, ali okonzekera nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Asilikali pafupifupi 40,000 anawoloka napita kukayima mʼchigwa cha Yeriko kukonzekera nkhondo. Onani mutuwo |