Yoswa 4:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi hafu la fuko la Manase anaoloka ndi zida zao pamaso pa ana a Israele, monga Mose adanena nao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi gawo lija la fuko la Manase anaoloka ndi zida zao pamaso pa ana a Israele, monga Mose adanena nao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu a fuko la Rubeni ndi la Gadi ndi theka la Manase, ndiwo adaoloka poyamba, ali okonzekera nkhondo, monga momwe Mose adaŵauzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu a fuko la Rubeni, Gadi ndi theka la fuko la Manase anawoloka patsogolo pa Aisraeli ali ndi zida, monga momwe Mose anawalamulira. Onani mutuwo |