Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoswa 4:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo kunali, utatha kuoloka Yordani mtundu wonse, Yehova ananena ndi Yoswa, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo kunali, utatha kuoloka Yordani mtundu wonse, Yehova ananena ndi Yoswa, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mtundu wonse wa Aisraele utaoloka Yordani, Chauta adauza Yoswa kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Anthu onse atatha kuwoloka Yorodani, Yehova anati kwa Yoswa,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 4:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo kudzali, tsiku lakuoloka inu Yordani kulowa dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, kuti mudziutsire miyala yaikulu, ndi kuimata ndi njeresa;


Pamenepo munaoloka Yordani, ndi kufika ku Yeriko; ndi eni ake a ku Yeriko anaponyana nanu nkhondo, Aamori, ndi Aperizi, ndi Akanani, ndi Ahiti, ndi Agirigasi, Ahivi, ndi Ayebusi; ndipo ndinawapereka m'dzanja lanu.


Ndipo ansembe akulisenza likasa la chipangano la Yehova, anaima pouma pakati pa Yordani, ndi Aisraele onse anaoloka pouma mpaka mtundu wonse unatha kuoloka Yordani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa