Yoswa 4:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo kunali, utatha kuoloka Yordani mtundu wonse, Yehova ananena ndi Yoswa, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo kunali, utatha kuoloka Yordani mtundu wonse, Yehova ananena ndi Yoswa, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mtundu wonse wa Aisraele utaoloka Yordani, Chauta adauza Yoswa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Anthu onse atatha kuwoloka Yorodani, Yehova anati kwa Yoswa, Onani mutuwo |