Yoswa 3:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yoswa ananena kwa anthu, Mudzipatule, pakuti mawa Yehova adzachita zodabwitsa pakati pa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yoswa ananena kwa anthu, Mudzipatule, pakuti mawa Yehova adzachita zodabwitsa pakati pa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero Yoswa adauza anthu onse kuti, “Mudzisungetu tsono, chifukwa maŵa Chauta adzachita zodabwitsa zazikulu pakati panu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yoswa anawuza anthu kuti, “Dzipatuleni tsono pakuti mawa Yehova adzachita zodabwitsa pakati panu.” Onani mutuwo |