Yoswa 3:10 - Buku Lopatulika10 Nati Yoswa, Ndi ichi mudzadziwa kuti Mulungu wamoyo ali pakati pa inu, ndi kuti adzapirikitsa ndithu pamaso panu Akanani, ndi Ahiti, ndi Ahivi, ndi Aperizi, ndi Agirigasi, ndi Aamori, ndi Ayebusi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nati Yoswa, Ndi ichi mudzadziwa kuti Mulungu wamoyo ali pakati pa inu, ndi kuti adzapirikitsa ndithu pamaso panu Akanani, ndi Ahiti, ndi Ahivi, ndi Aperizi, ndi Agirigasi, ndi Aamori, ndi Ayebusi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Motero mudzadziŵa kuti Mulungu wamoyo ali pakati panu. Inu mukamapita patsogolo, Iye adzapirikitsa Akanani onse, pamodzi ndi Ahiti, Ahivi, Aperizi, Agirigasi, Aamori ndi Ayebusi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Umu ndi mmene mudzadziwira kuti Mulungu wamoyo ali pakati panu. Inu mukamadzapita patsogolo Iye adzathamangitsa Akanaani, Ahiti, Ahivi, Aperezi, Agirigasi, Aamori ndi Ayebusi. Onani mutuwo |