Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 24:4 - Buku Lopatulika

4 Ndi kwa Isaki ndinapatsa Yakobo ndi Esau, ndipo ndinampatsa Esau phiri la Seiri likhale lakelake; koma Yakobo ndi ana ake anatsikira kunka ku Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndi kwa Isaki ndinapatsa Yakobo ndi Esau, ndipo ndinampatsa Esau phiri la Seiri likhale lakelake; koma Yakobo ndi ana ake anatsikira kunka ku Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 ndipo Isakiyo ndidampatsa Yakobe ndi Esau. Dziko lamapiri la Seiri ndidapatsa Esau kuti likhale choloŵa chake, koma Yakobe ndi ana ake adatsikira ku Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 ndipo Isake ndinamupatsa Yakobo ndi Esau. Ndinapereka dziko la mapiri la Seiri kwa Esau, koma Yakobo ndi ana ake anapita ku Igupto.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 24:4
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anatumiza amithenga patsogolo pake kwa Esau mkulu wake, ku dziko la Seiri, kudera la ku Edomu.


Ndipo Esau anakhala m'phiri la Seiri; Esau ndiye Edomu.


Mibadwo ya Esau atate wao wa Aedomu m'phiri la Seiri ndi iyi:


Pamenepo Israele analowa mu Ejipito; ndi Yakobo anakhala mlendo m'dziko la Hamu.


Taonani, ana ndiwo cholowa cha kwa Yehova; chipatso cha m'mimba ndicho mphotho yake.


Ndipo Yakobo anatsikira ku Ejipito; ndipo anamwalira, iye ndi makolo athu;


musalimbana nao; popeza sindikupatsakoni dziko lao, pangakhale popondapo phazi lanu ai; pakuti ndapatsa Esau phiri la Seiri likhale lakelake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa