Yoswa 22:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi hafu la fuko la Manase anabwerera, nachoka kwa ana a Israele ku Silo, ndiwo wa m'dziko la Kanani kunka ku dziko la Giliyadi, ku dziko laolao, limene anakhala eni ake, monga mwa lamulo la Yehova, mwa dzanja la Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi fuko la Manase logawika pakati anabwerera, nachoka kwa ana a Israele ku Silo, ndiwo wa m'dziko la Kanani kunka ku dziko la Giliyadi, ku dziko laolao, limene anakhala eni ake, monga mwa lamulo la Yehova, mwa dzanja la Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Motero anthu onse a fuko la Rubeni ndi la Gadi, pamodzi ndi theka lija la fuko la Manase, adabwerera kwao. Aisraele ena onse adaŵasiya ku Silo m'dziko la Kanani, ndipo iwowo adapita ku dziko la Giliyadi. Dziko limeneli ndilo linali lao, chifukwa adalilandira potsata malamulo a Chauta kudzera mwa Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho mafuko a Rubeni, Gadi, pamodzi ndi theka la fuko la Manase anabwerera kwawo. Aisraeli ena onse anawasiya ku Silo mʼdziko la Kanaani. Tsono anapita ku dziko la Giliyadi, dziko limene linali lawo popeza analilandira potsata malamulo a Yehova kudzera mwa Mose. Onani mutuwo |