Yoswa 22:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo tsopano Yehova Mulungu wanu wapumitsa abale anu, monga adanena nao; potero bwererani tsopano, mukani ku mahema anu, ku dziko la cholowa chanu chimene Mose mtumiki wa Yehova anakuninkhani tsidya lija la Yordani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo tsopano Yehova Mulungu wanu wapumitsa abale anu, monga adanena nao; potero bwererani tsopano, mukani ku mahema anu, ku dziko la cholowa chanu chimene Mose mtumiki wa Yehova anakuninkhani tsidya lija la Yordani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsopano Chauta, Mulungu wanu, wapatsa mtendere Aisraele anzanu, monga momwe adaalonjezera. Motero bwererani kwanu ku dziko limene mudalandira, dziko limene lili patsidya pa mtsinje wa Yordani kuvuma, limene Mose mtumiki wa Chauta adakupatsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono pakuti Yehova Mulungu wanu wapereka mpumulo kwa abale anu monga anayankhulira nawo, bwererani ku nyumba zanu ku dziko limene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani, dziko limene lili pa tsidya la Yorodani kummawa. Onani mutuwo |