Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 22:2 - Buku Lopatulika

2 nanena nao, Mwasunga inu zonsezo anakulamulirani Mose mtumiki wa Yehova; mwamveranso mau anga m'zonse ndinakulamulirani inu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 nanena nao, Mwasunga inu zonsezo anakulamulirani Mose mtumiki wa Yehova; mwamveranso mau anga m'zonse ndinakulamulirani inu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndipo adaŵauza kuti, “Zonse zimene Mose mtumiki wa Chauta adakulamulani kuti muchite, mwachitadi, ndipo mwamvera malamulo anga onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 ndipo anawawuza kuti, “Inu mwachita zonse zimene Mose mtumiki wa Yehova anakulamulani, ndipo mwamvera mu zonse zimene ndinakulamulirani.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 22:2
4 Mawu Ofanana  

simunasiye abale anu masiku awa ambiri mpaka lero lino, koma mwasunga chisungire lamulo la Yehova Mulungu wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa