Yoswa 22:12 - Buku Lopatulika12 Pamene ana a Israele anamva ichi msonkhano wonse wa ana a Israele anasonkhana ku Silo, kuti awakwerere kuwathira nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamene ana a Israele anamva ichi msonkhano wonse wa ana a Israele anasonkhana ku Silo, kuti awakwerere kuwathira nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono Aisraele atamva zimenezi, onse pamodzi adasonkhana ku Silo, kuti apite kukamenyana nawo nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 gulu lonse la Aisraeli linasonkhana ku Silo kuti lipite kukachita nawo nkhondo. Onani mutuwo |