Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 22:12 - Buku Lopatulika

12 Pamene ana a Israele anamva ichi msonkhano wonse wa ana a Israele anasonkhana ku Silo, kuti awakwerere kuwathira nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pamene ana a Israele anamva ichi msonkhano wonse wa ana a Israele anasonkhana ku Silo, kuti awakwerere kuwathira nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono Aisraele atamva zimenezi, onse pamodzi adasonkhana ku Silo, kuti apite kukamenyana nawo nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 gulu lonse la Aisraeli linasonkhana ku Silo kuti lipite kukachita nawo nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 22:12
9 Mawu Ofanana  

Pakuti ndiwachitira iwo umboni kuti ali ndi changu cha kwa Mulungu, koma si monga mwa chidziwitso.


muzikanthatu okhala m'mzinda muja ndi lupanga lakuthwa; ndi kuononga konse, ndi zonse zili m'mwemo, ng'ombe zake zomwe, ndi lupanga lakuthwa.


Ndipo msonkhano wonse wa ana a Israele unasonkhana ku Silo, nuutsa komweko chihema chokomanako; ndipo dziko linawagonjera.


Ndipo ana a Israele anatumiza kwa ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi hafu la fuko la Manase, ku dziko la Giliyadi, Finehasi mwana wa Eleazara wansembe,


M'mene anafika kwa ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi hafu la fuko la Manase, ku dziko la Giliyadi, ananena nao ndi kuti,


Ndipo Finehasi mwana wa Eleazara wansembe, ndi akalonga anabwerera kuchokera kwa ana a Rubeni, ndi kwa ana a Gadi, m'dziko la Giliyadi, kudza ku dziko la Kanani kwa ana a Israele, nawabwezera mau.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa