Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 22:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo Yoswa anaitana Arubeni ndi Agadi, ndi hafu la fuko la Manase,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo Yoswa anaitana Arubeni ndi Agadi, ndi fuko la Manase logawika pakati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Pambuyo pake Yoswa adaitana anthu a fuko la Rubeni ndi la Gadi, ndi hafu lina lija la fuko la Manase wakuvuma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pambuyo pake Yoswa anayitanitsa fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 22:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anadzisankhira gawo loyamba, popeza kumeneko kudasungika gawo la wolamulira; ndipo anadza ndi mafumu a anthu, anachita chilungamo cha Yehova, ndi maweruzo ake ndi Israele.


Ndipo Yoswa anati kwa Arubeni, ndi Agadi, ndi hafu la fuko la Manase, ndi kuti,


mpaka Yehova atapatsa abale anu mpumulo, monga umo anakuninkhirani inu, naonso alandira dzikolo awaninkha Yehova Mulungu wanu; pamenepo mubwerere ku dziko lanulanu, ndi kukhala nalo, limene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani tsidya lino la Yordani la kum'mawa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa