Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 21:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo anapatsa motapa pa fuko la ana a Yuda, ndi pa fuko la ana a Simeoni, mizinda iyi yotchulidwa maina ao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo anapatsa motapa pa fuko la ana a Yuda, ndi pa fuko la ana a Simeoni, midzi iyi yotchulidwa maina ao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Mizinda ya Yuda ndi Simeoni imene idapatsidwa

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Awa ndi mayina a mizinda ya mafuko a Yuda ndi Simeoni imene inaperekedwa kwa zidzukulu za Aaroni,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 21:9
7 Mawu Ofanana  

Ndi mbale wake Asafu wokhala ku dzanja lake lamanja, ndiye Asafu mwana wa Berekiya, mwana wa Simea,


Ndipo anapatsa mwamaere, motapa pa fuko la ana a Yuda, ndi pa fuko la Simeoni, ndi pa fuko la ana a Benjamini, mizinda iyi yotchulidwa maina ao.


Ndi omvera iye ndiwo Edeni, ndi Miniyamini, ndi Yesuwa, ndi Semaya, Amariya ndi Sekaniya, m'mizinda ya ansembe, kugawira abale ao m'zigawo zao mokhulupirika, akulu monga ang'ono;


kuti ikhale ya ana a Aroni a mabanja a Akohati, a ana a Levi, pakuti maere oyamba adatulukira iwowa.


Ndipo maere anatulukira mabanja a Akohati; ndipo molota maere ana a Aroni wansembe, ndiwo Alevi, analandira motapa pa fuko la Yuda, ndi pa fuko la Simeoni, ndi pa fuko la Benjamini, mizinda khumi ndi itatu.


Motero ana a Israele anapatsa Alevi mizinda iyi ndi mabusa ao, molota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa