Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 21:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo ana a Israele anapatsa Alevi, kutapa pa cholowa chao, monga mwa lamulo la Yehova, mizinda iyi ndi mabusa ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo ana a Israele anapatsa Alevi, kutapa pa cholowa chao, monga mwa lamulo la Yehova, midzi iyi ndi mabusa ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Motero Aisraele adapatsa Aleviwo mizindayo pochita maere, pamodzi ndi mabusa a zoŵeta, kuchokera pa magawo ao omwewo, potsata zomwe Chauta adalamula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Choncho, Aisraeli anapereka kwa fuko la Levi mizinda iyi pamodzi ndi malo owetera ziweto zawo kuchokera ku madera awo, monga Yehova analamulira:

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 21:3
7 Mawu Ofanana  

Kutembereredwe kukwiya kwao, chifukwa kunali koopsa; ndi kupsa mtima kwao, chifukwa kunali kwankhalwe. Ndidzawagawanitsa mu Yakobo. Ndidzabalalitsa iwo mu Israele.


Midzi yonse muipereke kwa Alevi ndiyo mizinda makumi anai ndi isanu ndi itatu, iyo pamodzi ndi mabusa ao.


nanena nao ku Silo m'dziko la Kanani, ndi kuti Yehova analamulira mwa dzanja la Mose kuti atipatse mizinda yokhalamo ife, ndi mabusa a zoweta zathu.


Ndipo maere anatulukira mabanja a Akohati; ndipo molota maere ana a Aroni wansembe, ndiwo Alevi, analandira motapa pa fuko la Yuda, ndi pa fuko la Simeoni, ndi pa fuko la Benjamini, mizinda khumi ndi itatu.


Mizinda yonse ya Alevi, pakati pa cholowa cha ana a Israele ndiyo mizinda makumi anai kudza isanu ndi itatu, ndi mabusa ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa