Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 21:2 - Buku Lopatulika

2 nanena nao ku Silo m'dziko la Kanani, ndi kuti Yehova analamulira mwa dzanja la Mose kuti atipatse mizinda yokhalamo ife, ndi mabusa a zoweta zathu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 nanena nao ku Silo m'dziko la Kanani, ndi kuti Yehova analamulira mwa dzanja la Mose kuti atipatse midzi yokhalamo ife, ndi mabusa a zoweta zathu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Aleviwo adafika ku Silo m'dziko la Kanani, nanena kuti, “Chauta adalamula kudzera mwa Mose kuti ife atipatse mizinda yokhalamo, ndiponso atipatse mabusa pozungulira mizindayo, kuti tizidyetsapo zoŵeta zathu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 ku Silo mʼdziko la Kanaani ndipo anati, “Yehova analamula kudzera mwa Mose kuti atipatse mizinda kuti tikhalemo, pamodzi ndi malo odyetseramo ziweto zathu.”

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 21:2
9 Mawu Ofanana  

Kunena za mizinda ya Alevi, nyumba za m'mizinda yaoyao, Alevi akhoza kuziombola nthawi zonse.


kapena thumba la kamba la kunjira, kapena malaya awiri, kapena nsapato, kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira zakudya zake.


Koma iye amene aphunzira mau, ayenera kuchereza womphunzitsayo m'zonse zabwino.


Monga Yehova analamulira Mose, momwemo ana a Israele anachita, nagawana dziko.


Ndipo msonkhano wonse wa ana a Israele unasonkhana ku Silo, nuutsa komweko chihema chokomanako; ndipo dziko linawagonjera.


Ndipo ana a Israele anapatsa Alevi, kutapa pa cholowa chao, monga mwa lamulo la Yehova, mizinda iyi ndi mabusa ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa