Yoswa 20:3 - Buku Lopatulika3 Kuti athawireko wakupha munthu osamupha dala, osadziwa; ndipo idzakhalire inu yopulumukirako, kumpulumuka wolipsa mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kuti athawireko wakupha munthu osamupha dala, osadziwa; ndipo idzakhalire inu yopulumukirako, kumpulumuka wolipsa mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Munthu aliyense wopha mnzake mwangozi, osati mwadala, angathe kuthaŵira kumeneko. Motero angathe kupulumuka kwa wofuna kumlipsira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 kuti aliyense amene wapha munthu mosazindikira osati mwadala azithawirako. Motero adzatetezedwa kwa wolipsira. Onani mutuwo |