Yoswa 20:2 - Buku Lopatulika2 Nena ndi ana a Israele ndi kuti, Mudziikire mizinda yopulumukirako, monga ndinanena kwa inu mwa dzanja la Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nena ndi ana a Israele ndi kuti, Mudziikire midzi yopulumukirako, monga ndinanena kwa inu mwa dzanja la Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza Aisraele kuti, ‘Sankhulani mizinda yopulumukiramo, imene Ine ndidakuuzani kudzera mwa Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Uza Aisraeli kuti apatule mizinda yopulumukiramo, monga ine ndinakulangizira kudzera mwa Mose, Onani mutuwo |