Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 2:8 - Buku Lopatulika

8 Koma asanagone iwo, anawakwerera patsindwi iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Koma asanagone iwo, anawakwerera patsindwi iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono azondiwo asanagone, Rahabu adakwera padengapo

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Azondiwo asanagone, Rahabe anakwera pa denga

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 2:8
4 Mawu Ofanana  

Koma adawakweretsa patsindwi, nawabisa ndi mitengo yanthamza yoyanika patsindwi.


Ndipo amunawo anawalondola panjira ya ku Yordani yonka kudooko; ndipo atatuluka akuwalondola, anatseka pachipata.


nati kwa amunawo, Ndidziwa kuti Yehova wakupatsani dzikoli, ndi kuti kuopsa kwanu kwatigwera, ndi kuti okhala m'dziko onse asungunuka pamaso panu.


Koma nyumbayi inadzala ndi amuna ndi akazi; ndi akalonga onse a Afilisti anali momwemo ndi patsindwi panali amuna ndi akazi ngati zikwi zitatu akuyang'ana pakusewera Samisoni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa