Yoswa 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo amunawo anawalondola panjira ya ku Yordani yonka kudooko; ndipo atatuluka akuwalondola, anatseka pachipata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo amunawo anawalondola pa njira ya ku Yordani yonka kudooko; ndipo atatuluka akuwalondola, anatseka pachipata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Atangochoka anthu otumidwa ndi mfumuwo kutuluka mumzindamo, chipata chidatsekedwa. Ndipo adapita ku mseu kukaŵafunafuna azondiwo, mpaka adakafika ku dooko la Yordani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nthumwi za mfumu zija zitatuluka ndipo chipata chinatsekedwa. Nthumwizo zinapita kukawafunafuna azondi aja mpaka ku dooko la Yorodani. Onani mutuwo |