Yoswa 2:5 - Buku Lopatulika5 ndipo m'mene akadati atseke pachipata, kutada, anatuluka amunawo; uko anamuka amunawo osakudziwa ine; muwalondole msanga, pakuti mudzawapeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo m'mene akadati atseke pachipata, kutada, anatuluka amunawo; uko anamuka amunawo osakudziwa ine; muwalondole msanga, pakuti mudzawapeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kuno achoka ndi chisisira, chipata cha mzinda uno chili pafupi kutsekedwa. Sindidaŵafunse kumene akupita, koma mukaŵalondola, mungathe kuŵapeza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iwo achoka kuno ndi chisisira, chipata cha mzinda chili pafupi kutsekedwa. Ndiye sindidziwa kumene alowera. Koma mukawalondola msanga muwapeza.” Onani mutuwo |