Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 19:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anali nacho cholowa chao Beereseba, kapena Sheba, ndi Molada;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anali nacho cholowa chao Beereseba, kapena Sheba, ndi Molada;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndipo lidaphatikiza Beereseba, Molada,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Dzikolo linaphatikiza zigawo izi: Beeriseba (ndi Seba), Molada,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 19:2
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa, natenga mkate ndi thumba la madzi, nampatsa Hagara, naika paphewa pake, ndi mwana, namchotsa iye: ndipo iye anamuka, nasocherera m'chipululu cha Beereseba.


Chifukwa chake anatcha malowo Beereseba: chifukwa pamenepo analumbira onse awiri.


Amama ndi Sema ndi Molada;


ndi Hazara-Suwala, ndi Beereseba, ndi Biziyotiya;


Ndipo maere achiwiri anamtulukira Simeoni, fuko la ana a Simeoni monga mwa mabanja ao; ndi cholowa chao chinali pakati pa cholowa cha ana a Yuda.


ndi Hazara-Suwala, ndi Bala, ndi Ezemu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa