Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 19:16 - Buku Lopatulika

16 Ichi ndi cholowa cha ana a Zebuloni monga mwa mabanja ao, mizinda iyi ndi midzi yao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ichi ndi cholowa cha ana a Zebuloni monga mwa mabanja ao, midzi iyi ndi milaga yao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake inali m'dziko limene mabanja a fuko la Zebuloni adalandira ngati choloŵa chao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake ndi imene mabanja a fuko la Zebuloni analandira.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 19:16
2 Mawu Ofanana  

ndi Katati, ndi Nahalala ndi Simironi, ndi Idala ndi Betelehemu: mizinda khumi ndi iwiri ndi midzi yao.


Maere achinai anamtulukira Isakara, kunena za ana a Isakara monga mwa mabanja ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa