Yoswa 19:11 - Buku Lopatulika11 nakwera malire ao kunka kumadzulo ndi ku Mareyala nafikira ku Dabeseti, nafikira ku mtsinje wa patsogolo pa Yokoneamu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 nakwera malire ao kunka kumadzulo ndi ku Mareyala nafikira ku Dabeseti, nafikira ku mtsinje wa patsogolo pa Yokoneamu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono malirewo adakwera naloŵa kuzambwe ku Mareyala, nakafika ku Debeseti ndi ku mtsinje wa kuvuma kwa Yokoneamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Malirewo anakwera kupita cha kumadzulo ku Marala nakafika ku Dabeseti ndi ku mtsinje wa kummawa kwa Yokineamu. Onani mutuwo |