Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 18:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anatsala mwa ana a Israele mafuko asanu ndi awiri osawagawira cholowa chao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anatsala mwa ana a Israele mafuko asanu ndi awiri osawagawira cholowa chao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Nthaŵi imeneyo nkuti mafuko asanu ndi aŵiri asanapatsidwe magawo ao a dzikolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Koma pa nthawiyo nʼkuti mafuko asanu ndi awiri a Aisraeli asanalandire cholowa chawo.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 18:2
2 Mawu Ofanana  

Ndipo msonkhano wonse wa ana a Israele unasonkhana ku Silo, nuutsa komweko chihema chokomanako; ndipo dziko linawagonjera.


Ndipo Yoswa anati kwa ana a Israele, Muchedwa mpaka liti kulowa ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa