Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 17:9 - Buku Lopatulika

9 Natsikira malire ku mtsinje wa Kana, kumwera kwa mtsinje; mizinda iyi inakhala ya Efuremu pakati pa mizinda ya Manase; ndi malire a Manase anali kumpoto kwa mtsinje; ndi matulukiro ake anali kunyanja;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Natsikira malire ku mtsinje wa Kana, kumwera kwa mtsinje; midzi iyi inakhala ya Efuremu pakati pa midzi ya Manase; ndi malire a Manase anali kumpoto kwa mtsinje; ndi matulukiro ake anali kunyanja;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsono malire ake adatsikira ku kamtsinje ka Kana. Mizinda yakumwera kwa kamtsinje kameneka inali ya fuko la Efuremu, ngakhale inali m'dziko la Manase. Malire a dziko la Manase adalambalala chakumpoto kwa kamtsinjeko, nakalekezera ku nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ndipo malire ake anapitirira kummwera mpaka ku mtsinje wa ku Kana. Mizinda ya kummwera kwa mtsinjewo inali ya fuko la Efereimu ngakhale kuti inali mʼdziko la Manase. Malire a fuko la Manase anapita kumpoto kwa mtsinje wa Kana ndi kukathera ku Nyanja.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 17:9
4 Mawu Ofanana  

natsikira kumadzulo kunka ku malire a Ayafileti, ku malire a Betehoroni wa kunsi, ndi ku Gezere; ndi matulukiro ake anali kunyanja.


kumwera nkwa Efuremu ndi kumpoto nkwa Manase, ndi malire ake ndi nyanja; ndi kumpoto anakomana ndi Asere, ndi kum'mawa anakomana ndi Isakara.


nazungulira malire kunka ku Rama, ndi kumzinda wa linga la Tiro; nazungulira malire kunka ku Hosa; ndi matulukiro ake anali kunyanja, kuchokera ku Mahalabu mpaka ku Akizibu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa