Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 17:8 - Buku Lopatulika

8 Dziko la Tapuwa linali la Manase; koma Tapuwa mpaka malire a Manase linakhala la ana a Efuremu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Dziko la Tapuwa linali la Manase; koma Tapuwa mpaka malire a Manase linakhala la ana a Efuremu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Dzikolo linali la Manase, koma mzinda wa Tapuwa wapamalire unali wa fuko la Efuremu, ngakhale kuti m'pakati penipeni pa mizinda ya Manase.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 (Manase anatenga dziko la Tapuwa, koma mzinda wa Tapuwawo, umene unali mʼmalire mwa Manase unali wa fuko la Efereimu).

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 17:8
6 Mawu Ofanana  

Ndi m'malire a Manase, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Efuremu, limodzi.


mfumu ya ku Tapuwa, imodzi; mfumu ya ku Hefere, imodzi;


ndi Zanowa, ndi Enganimu, Tapuwa, ndi Enamu;


ndi Yanimu, ndi Betetapuwa, ndi Afeka;


Kuyambira ku Tapuwa malire anamuka kumadzulo ku mtsinje wa Kana; ndi matulukiro ake anali kunyanja. Ichi ndi cholowa cha fuko la ana a Efuremu monga mwa mabanja ao;


Ndipo malire a Manase anayambira ku Asere, kunka ku Mikametati, wokhala chakuno cha Sekemu; namuka malire ku dzanja lamanja kwa nzika za Enitapuwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa