Yoswa 17:6 - Buku Lopatulika6 popeza ana aakazi a Manase adalandira cholowa pakati pa ana ake aamuna; ndi dziko la Giliyadi linakhala la ana a Manase otsala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 popeza ana akazi a Manase adalandira cholowa pakati pa ana ake amuna; ndi dziko la Giliyadi linakhala la ana a Manase otsala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 popeza kuti ana aakazi a Manase ndi ana ake aamuna, onsewo adalandira magawo ao. Dziko la Giliyadi lidapatsidwa kwa otsala mwa zidzukulu za Manase. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 chifukwa ana aakazi a fuko la Manase analandira cholowa chawo pakati pa ana aamuna. Dziko la Giliyadi linali dziko la zidzukulu zonse za Manase. Onani mutuwo |