Yoswa 17:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anamgwera Manase magawo khumi, osawerenga dziko la Giliyadi ndi Basani lokhala tsidya lija la Yordani: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anamgwera Manase magawo khumi, osawerenga dziko la Giliyadi ndi Basani lokhala tsidya lija la Yordani: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Choncho kuwonjeza pa maiko a Giliyadi ndi Basani a kuvuma kwa Yordani, a fuko la Manase adalandiranso magawo khumi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Choncho kuwonjezera pa mayiko a Giliyadi ndi Basani kummawa kwa Yorodani, anthu a fuko la Manase analandiranso magawo khumi Onani mutuwo |