Yoswa 17:12 - Buku Lopatulika12 Koma ana a Manase sanathe kuingitsa a m'mizinda aja, popeza Akanani anafuna kukhala m'dziko lija. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma ana a Manase sanathe kuingitsa a m'midzi aja, popeza Akanani anafuna kukhala m'dziko lija. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Komabe anthu a fuko la Manase sadathe kuŵapirikitsa Akanani okhala m'mizinda imeneyo. Motero Akananiwo adangokhalabe komweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Komabe anthu a fuko la Manase sanathe kuwapirikitsa anthu okhala mʼmizinda imeneyi. Choncho Akanaani anakhalabe mʼmizindayi. Onani mutuwo |