Yoswa 16:9 - Buku Lopatulika9 pamodzi ndi mizinda adaipatulira ana a Efuremu pakati pa cholowa cha ana a Manase, mizinda yonse pamodzi ndi midzi yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 pamodzi ndi midzi adaipatulira ana a Efuremu pakati pa cholowa cha ana a Manase, midzi yonse pamodzi ndi milaga yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 kuphatikizapo mizinda ndi midzi yopatsidwa kwa Aefuremu, koma yokhala m'kati mwa dziko la anthu a fuko la Manase. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 kuphatikizapo mizinda yonse ndi midzi yake yopatsidwa kwa Efereimu, koma yokhala mʼkati mwa dziko la Manase. Onani mutuwo |