Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 16:4 - Buku Lopatulika

4 Motero ana a Yosefe, Manase ndi Efuremu analandira cholowa chao,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Motero ana a Yosefe, Manase ndi Efuremu analandira cholowa chao,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Choncho ana a Yosefe, Manase ndi Efuremu adalandira choloŵa chao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho Manase ndi Efereimu, ana a Yosefe analandira cholowa chawo.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 16:4
6 Mawu Ofanana  

Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga.


Atero Ambuye Yehova, Malire amene mugawe nao dziko likhale cholowa chao monga mwa mafuko khumi ndi awiri a Israele ndi awa: Yosefe akhale nao magawo awiri.


Pakuti ana a Yosefe ndiwo mafuko awiri, Manase ndi Efuremu; ndipo sanawagawire Alevi kanthu m'dziko, koma mizinda yokhalamo ndi dziko lozungulirako likhale la zoweta zao ndi chuma chao.


Ndipo malire a ana a Efuremu, monga mwa mabanja ao, ndiwo: malire a cholowa chao kum'mawa ndiwo Ataroti-Adara, mpaka Betehoroni wa kumtunda;


Pamenepo ana a Yosefe ananena ndi Yoswa, ndi kuti, Watipatsiranji cholowa chathu chamaere chimodzi ndi gawo limodzi, popeza ife ndife anthu aunyinji, pakuti Yehova anatidalitsa ndi pano pomwe?


Ndipo adzaligawa magawo asanu ndi awiri; Yuda adzakhala m'malire ake kumwera, ndi a m'nyumba ya Yosefe adzakhala m'malire mwao kumpoto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa