Yoswa 16:2 - Buku Lopatulika2 natuluka ku Betele kunka ku Luzi, napitirira kunka ku malire a Aariki, ku Ataroti; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 natuluka ku Betele kunka ku Luzi, napitirira kunka ku malire a Aariki, ku Ataroti; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kuchokera ku Betele malire ake adakafika ku Luzi, nabzola ku Ataroti kumene kunkakhala Aaraki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kuchokera ku Beteli malire ake anakafika ku Luzi, kudutsa dziko la Ataroti kumene kumakhala Aariki. Onani mutuwo |