Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 16:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo gawo la ana a Yosefe linatuluka kuchokera ku Yordani ku Yeriko, ku madzi a Yeriko kum'mawa, kuchipululu, nakwera kuchokera ku Yeriko kunka kumapiri ku Betele;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo gawo la ana a Yosefe linatuluka kuchokera ku Yordani ku Yeriko, ku madzi a Yeriko kum'mawa, kuchipululu, nakwera kuchokera ku Yeriko kunka kumapiri ku Betele;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Dziko limene lidapatsidwa kwa zidzukulu za Yosefe lidayambira ku mtsinje wa Yordani pafupi ndi Yeriko, cha kuvuma kwa akasupe a Yeriko, kukaloŵa m'chipululu. Lidayambiranso ku Yeriko, ndi kukaloŵa m'dziko lamapiri chakuzambwe, mpaka kukafika ku chipululu cha Betele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Dziko limene linapatsidwa kwa fuko la Yosefe linayambira ku mtsinje wa Yorodani ku Yeriko, kummawa kwa akasupe a Yeriko, ndiponso kuyambira mtsinje wa Yorodaniwo nʼkumakwera, kudutsa mʼchipululu mpaka ku mapiri a ku Beteli.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 16:1
10 Mawu Ofanana  

ana aamuna a Rakele: ndiwo Yosefe ndi Benjamini;


Ndi m'malire a Manase, kuyambira mbali ya kum'mawa kufikira mbali ya kumadzulo; Efuremu, limodzi.


M'chipululu, Betaraba, Midini, ndi Sekaka;


Ndipo malire ao a kumpoto anachokera ku Yordani; ndi malire anakwera ku mbali ya Yeriko kumpoto, nakwera pakati pa mapiri kumadzulo; ndi matulukiro ake anali ku chipululu cha Betaveni.


Ndipo adzaligawa magawo asanu ndi awiri; Yuda adzakhala m'malire ake kumwera, ndi a m'nyumba ya Yosefe adzakhala m'malire mwao kumpoto.


Ndipo Yoswa ndi Aisraele onse anaoneka ngati a ku Ai alikuwathyola, nathawira njira ya kuchipululu.


Ndipo anakwera iwo a m'nyumba ya Yosefe, naonso kunka ku Betele; ndipo Yehova anakhala nao.


Ndipo iwo a m'nyumba ya Yosefe anatumiza ozonda ku Betele. Koma kale dzina la mzindawo ndilo Luzi.


Anatumiza kwa iwo a ku Betele, ndi kwa iwo a ku Ramoti wa kumwera, ndi kwa iwo a ku Yatiri;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa