Yoswa 15:6 - Buku Lopatulika6 nakwera malire kunka ku Betehogila, napitirira kumpoto kwa Betaraba; nakwera malire kunka ku mwala wa Bohani mwana wa Rubeni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 nakwera malire kunka ku Betehogila, napitirira kumpoto kwa Betaraba; nakwera malire kunka ku mwala wa Bohani mwana wa Rubeni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 napitirira mpaka ku Betehogila, nakafika kumpoto kwa Betaraba. Adapitirira mpaka kukafika ku Mwala wa Bohani, mwana wa Rubeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 napitirira mpaka ku Beti-Hogila ndi kupitirira kumpoto mpaka ku Beti-Araba. Anapitirira mpaka anakafika ku Mwala wa Bohani. Onani mutuwo |