Yoswa 15:41 - Buku Lopatulika41 ndi Gederoti, Betedagoni, ndi Naama, ndi Makeda; mizinda khumi ndi isanu ndi umodzi pamodzi ndi midzi yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 ndi Gederoti, Betedagoni, ndi Naama, ndi Makeda; midzi khumi ndi isanu ndi umodzi pamodzi ndi milaga yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Gederoti, Betedagoni, Naama ndiponso Makeda. Yonse inali mizinda 16, pamodzi ndi midzi yake yozungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Gederoti, Beti-Dagoni, Naama ndi Makeda. Mizinda yonse pamodzi inalipo 16 pamodzi ndi midzi yake yozungulira. Onani mutuwo |