Yoswa 15:4 - Buku Lopatulika4 napitirira ku Azimoni, natuluka ku mtsinje wa Ejipito; ndi malekezero a malirewa anali ku Nyanja Yaikulu; awa ndi malire anu a kumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 napitirira ku Azimoni, natuluka ku mtsinje wa Ejipito; ndi malekezero a malirewa anali ku Nyanja Yaikulu; awa ndi malire anu a kumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adapitirira mpaka ku Azimoni, natsata mtsinje wa m'malire a Ejipito mpaka ku nyanja. Ameneŵa ndiwo malire akumwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anapitirira mpaka ku Azimoni motsata mtsinje umene uli malire a Igupto mpaka ku nyanja. Awa ndiwo malire awo a kummwera. Onani mutuwo |