Yoswa 15:2 - Buku Lopatulika2 Ndi malire ao a kumwera, anayambira ku malekezero a Nyanja ya Mchere, ku nyondo yoloza kumwera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndi malire ao a kumwera, anayambira ku malekezero a Nyanja ya Mchere, ku nyondo yoloza kumwera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Malire ake akumwera adayambira kumwera kwenikweni kwa Nyanja Yakufa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Malire awo a kummwera anayambira kummwera kwenikweni kwa Nyanja ya Mchere, Onani mutuwo |