Yoswa 15:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo gawo la fuko la ana a Yuda monga mwa mabanja ao linafikira malire a Edomu, ku chipululu cha Zini kumwera, ku malekezero a kumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo gawo la fuko la ana a Yuda monga mwa mabanja ao linafikira malire a Edomu, ku chipululu cha Zini kumwera, ku malekezero a kumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mabanja onse a fuko la Yuda adalandira chigawo cha dzikolo motero: dziko lao lidalekeza ku malire a Edomu, mpaka ku chipululu cha Zini, kumwera kwenikweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Chigawo cha dzikolo chimene mabanja a fuko la Yuda analandira chinafika ku malire ndi Edomu mpaka ku chipululu cha Zini kummwera kwenikweni. Onani mutuwo |