Yoswa 14:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti Mose adapatsa mafuko awiri, ndi fuko la hafu, cholowa tsidya ilo la Yordani; koma sanapatse Alevi cholowa pakati pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti Mose adapatsa mafuko awiri, ndi fuko logawika pakati, cholowa tsidya ilo la Yordani; koma sanapatse Alevi cholowa pakati pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mose adagaŵira mafuko aŵiri ndi theka aja magawo ao a dziko kuvuma kwa Yordani, koma Alevi okha sadaŵagaŵire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mose anapereka kwa mafuko awiri ndi theka dziko la kummawa kwa Yorodani, koma fuko la Levi lokha silinagawiridwe malo. Onani mutuwo |