Yoswa 14:2 - Buku Lopatulika2 Cholowa chao chinachitika ndi kulota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose, kunena za mafuko asanu ndi anai ndi fuko la hafu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kulandira kwao kunachitika ndi kulota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose, kunena za mafuko asanu ndi anai ndi fuko logawika pakati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Potsata zimene Mulungu adalamula Mose, dziko lonse lidagaŵidwa mwamaere kwa mafuko asanu ndi anai ndi theka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Madera anagawidwa mwa maere kwa mafuko asanu ndi anayi ndi theka, monga momwe Yehova analamulira kudzera mwa Mose. Onani mutuwo |