Yoswa 13:8 - Buku Lopatulika8 Pamodzi ndi iye Arubeni ndi Agadi analandira cholowa chao, chimene Mose adawapatsa tsidya ilo la Yordani kum'mawa, monga Mose mtumiki wa Yehova anawapatsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamodzi ndi iye Arubeni ndi Agadi analandira cholowa chao, chimene Mose adawapatsa tsidya ilo la Yordani kum'mawa, monga Mose mtumiki wa Yehova anawapatsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Anthu a fuko la Rubeni ndi la Gadi ndiponso theka lina lija la fuko la Manase adalandira dziko lao cha kuvuma kwa Yordani. Dziko limeneli ndilo lija adaŵapatsa Mose mtumiki wa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Anthu a fuko la Rubeni ndi fuko la Gadi pamodzi ndi theka lina la fuko la Manase analandira kale cholowa chawo chimene Mose mtumiki wa Yehova anawapatsa. Cholowa chawocho chinali kummawa kwa mtsinje wa Yorodani. Onani mutuwo |