Yoswa 13:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo tsopano uwagawire mafuko asanu ndi anai, ndi hafu la fuko la Manase, dziko ili likhale cholowa chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo tsopano uwagawire mafuko asanu ndi anai, ndi fuko la Manase logawika pakati, dziko ili likhale cholowa chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono ugaŵe maiko ameneŵa pakati pa mafuko asanu ndi anai ndi theka lina lija la fuko la Manase, kuti akhale choloŵa chao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsopano ugawire dziko limeneli mafuko asanu ndi anayi ndiponso theka la fuko la Manase, kuti likhale cholowa chawo.” Onani mutuwo |