Yoswa 13:6 - Buku Lopatulika6 nzika zonse za kumapiri kuyambira Lebanoni, mpaka Misirefoti-Maimu, Asidoni onse; ndidzawainga pamaso pa ana a Israele, koma limeneli uwagawire Aisraele, likhale cholowa chao, monga ndinakulamulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 nzika zonse za kumapiri kuyambira Lebanoni, mpaka Misirefoti-Maimu, Asidoni onse; ndidzawainga pamaso pa ana a Israele, koma limeneli uwagawire Aisraele, likhale cholowa chao, monga ndinakulamulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Palinso dziko la Asidoni, amene akukhala m'dera lamapiri, pakati pa phiri la Lebanoni ndi la Misirefoti-Maimu. Anthu onsewo Ine Mulungu ndidzaŵapirikitsa m'mene Aisraele azikafika. Uŵagaŵire Aisraele maiko ameneŵa kuti akhale choloŵa chao, potsata zomwe ndakulamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Palinso anthu okhala mʼchigawo cha ku mapiri kuchokera ku Lebanoni mpaka ku Misirefoti-Maimu, Ine ndidzawapirikitsa pamene Aisraeli azidzalowa. Tsono uwagawire Aisraeli dziko limeneli kuti likhale cholowa chawo monga momwe ndakulamulira. Onani mutuwo |