Yoswa 13:5 - Buku Lopatulika5 ndi dziko la Agebala, ndi Lebanoni, lonse kum'mawa, kuyambira Baala-Gadi pa tsinde la phiri la Heremoni, mpaka polowera pake pa Hamati; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi dziko la Agebala, ndi Lebanoni, lonse kum'mawa, kuyambira Baala-Gadi pa tsinde la phiri la Heremoni, mpaka polowera pake pa Hamati; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Palinso dziko lonse la Gebala ndi la Lebanoni chakuvuma, kuchokera ku Balagadi patsinde pa phiri la Heremoni mpaka ku Hamatipasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Palinso dziko lonse la Gebala ndi Lebanoni cha kummawa kuyambira ku Baala-Gadi pa tsinde pa phiri la Herimoni mpaka ku Lebo Hamati. Onani mutuwo |