Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 13:12 - Buku Lopatulika

12 ufumu wonse wa Ogi mu Basani, wa kuchita ufumu mu Asitaroti, ndi mu Ederei (yemweyo anatsala pa otsala a Arefaimu); pakuti Mose anakantha awa, nawainga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 ufumu wonse wa Ogi m'Basani, wa kuchita ufumu m'Asitaroti, ndi m'Ederei (yemweyo anatsala pa otsala a Arefaimu); pakuti Mose anakantha awa, nawainga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Ndipo ku Basani lidaphatikizapo dziko la Ogi amene ankalamula ku Asitaroti ndi ku Ederei. (Ogi anali yekhayo mfumu ya Arefaimu amene adatsalako). Mose anali atagonjetseratu anthu ameneŵa ndi kuŵapirikitsira kutali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Linaphatikizanso dziko la mfumu Ogi ya ku Basani imene imalamulira kuchokera ku Asiteroti ndi Ederi. Iye yekha ndiye anali mfumu ya Arefaimu amene anapulumuka. Mose anali atawagonjetsa anthu amenewa ndi kuwathamangitsira kutali.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 13:12
7 Mawu Ofanana  

atakantha Sihoni mfumu ya Aamori, wakukhala mu Hesiboni, ndi Ogi mfumu ya Basani, wakukhala mu Asitaroti, ku Ederei.


Nalandanso malire a Ogi mfumu ya Basani wotsala wa Arefaimu, wokhala ku Asitaroti ndi ku Ederei,


Koma ana a Israele sanainge Agesuri kapena Amaakati; koma Gesuri, ndi Maakati amakhala pakati pa Israele, mpaka lero lino.


ndi Giliyadi logawika pakati, ndi Asitaroti ndi Ederei, mizinda ya ufumu wa Ogi mu Basani, inali ya ana a Makiri mwana wa Manase, ndiwo ana a Makiri ogawika pakati, monga mwa mabanja ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa