Yoswa 13:10 - Buku Lopatulika10 ndi mizinda yonse ya Sihoni mfumu ya Aamori, wakuchita ufumu mu Hesiboni, mpaka malire a ana a Amoni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndi midzi yonse ya Sihoni mfumu ya Aamori, wakuchita ufumu m'Hesiboni, mpaka malire a ana a Amoni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Linkaphatikizaponso mizinda yonse yomwe inkalamulidwa ndi Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankalamula ku Hesiboni, mpaka ku malire a Aamoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Linkaphatikizanso mizinda yonse ya mfumu Sihoni ya Aamori, imene inkalamulira mu Hesiboni, mpaka ku malire a Aamoni. Onani mutuwo |