Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 12:9 - Buku Lopatulika

9 mfumu ya ku Yeriko, imodzi; mfumu ya ku Ai, ndiwo m'mbali mwa Betele, imodzi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 mfumu ya ku Yeriko, imodzi; mfumu ya ku Ai, ndiwo m'mbali mwa Betele, imodzi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Mafumu amene adagonjetsedwawo ndi aŵa: mafumu a ku Yeriko, Ai pafupi ndi Betele,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 mfumu ya Yeriko imodzi mfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 12:9
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo Yehova anati kwa Yoswa, Usaope, kapena kutenga nkhawa, tenga anthu onse a nkhondo apite nawe, ndipo tauka, kwera ku Ai; taona, ndapereka m'dzanja lako mfumu ya ku Ai, ndi anthu ake ndi mzinda wake ndi dziko lake;


Ndipo sanatsale mwamuna mmodzi yense mu Ai kapena mu Betele osatulukira kwa Israele; nasiya mzinda wapululu, napirikitsa Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa