Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 12:4 - Buku Lopatulika

4 Nalandanso malire a Ogi mfumu ya Basani wotsala wa Arefaimu, wokhala ku Asitaroti ndi ku Ederei,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Nalandanso malire a Ogi mfumu ya Basani wotsala wa Arefaimu, wokhala ku Asitaroti ndi ku Ederei,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Aisraele adagonjetsanso Ogi, mfumu ya ku Basani, amene anali mmodzi mwa otsala a Arefaimu. Iyeyu ankakhala ku Asitaroti ndi ku Ederei.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ogi mfumu ya mzinda wa Basani, amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 12:4
6 Mawu Ofanana  

atakantha Sihoni mfumu ya Aamori, wakukhala mu Hesiboni, ndi Ogi mfumu ya Basani, wakukhala mu Asitaroti, ku Ederei.


ufumu wonse wa Ogi mu Basani, wa kuchita ufumu mu Asitaroti, ndi mu Ederei (yemweyo anatsala pa otsala a Arefaimu); pakuti Mose anakantha awa, nawainga.


ndi Giliyadi logawika pakati, ndi Asitaroti ndi Ederei, mizinda ya ufumu wa Ogi mu Basani, inali ya ana a Makiri mwana wa Manase, ndiwo ana a Makiri ogawika pakati, monga mwa mabanja ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa