Yoswa 12:3 - Buku Lopatulika3 ndi pachidikha mpaka nyanja ya Kineroti kum'mawa, ndi mpaka nyanja ya kuchidikha, ndiyo Nyanja ya Mchere kum'mawa, njira ya Beteyesimoti; ndi kumwera pansi pa matsikiro a Pisiga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi pachidikha mpaka nyanja ya Kineroti kum'mawa, ndi mpaka nyanja ya kuchidikha, ndiyo Nyanja ya Mchere kum'mawa, njira ya Beteyesimoti; ndi kumwera pansi pa matsikiro a Pisiga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Dzikolo lidaphatikizaponso chigwa cha Yordani, kuyambira kumwera kwa nyanja ya Galilea, kumapita cha ku Beteyesimoti, mzinda umene uli pafupi pa Nyanja Yakufa, mpaka kumwera ndithu, patsinde pa phiri la Pisiga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga. Onani mutuwo |