Yoswa 12:2 - Buku Lopatulika2 Sihoni mfumu ya Aamori wokhala mu Hesiboni, wochita ufumu kuyambira ku Aroere ndiwo m'mphepete mwa chigwa cha Arinoni, ndi pakati pa chigwa ndi pa Giliyadi wogawika pakati, kufikira mtsinje wa Yaboki, ndiwo malire a ana a Amoni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Sihoni mfumu ya Aamori wokhala m'Hesiboni, wochita ufumu kuyambira ku Aroere ndiwo m'mphepete mwa chigwa cha Arinoni, ndi pakati pa chigwa ndi pa Giliyadi wogawika pakati, kufikira mtsinje wa Yaboki, ndiwo malire a ana a Amoni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Sihoni mfumu ya Aamori amene ankakhala ku Hesiboni. Iyeyu ankalamulira kuyambira ku Aroere, mzinda umene uli pafupi ndi mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki ku malire a dziko la Aamoni, ndiponso kuphatikizapo theka la dera la Giliyadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi. Onani mutuwo |